Zefaniya 2
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
2 Sonkhanani pamodzi, sonkhanani pamodzi,
inu mtundu wochititsa manyazi,
2 isanafike nthawi yachiweruzo,
nthawi yanu isanawuluke ngati mungu,
usanakufikeni mkwiyo woopsa wa Yehova,
tsiku la ukali wa Yehova lisanafike pa inu.
3 Funafunani Yehova, inu nonse odzichepetsa a mʼdziko,
inu amene mumachita zimene amakulamulani.
Funafunani chilungamo, funafunani kudzichepetsa;
mwina mudzatetezedwa
pa tsiku la mkwiyo wa Yehova.
Za Afilisti
4 Gaza adzasiyidwa
ndipo Asikeloni adzasanduka bwinja.
Nthawi yamasana Asidodi adzakhala wopanda anthu
ndipo Ekroni adzazulidwa.
5 Tsoka inu okhala mʼmbali mwa nyanja,
inu mtundu wa Akereti;
mawu a Yehova akutsutsa
iwe Kanaani, dziko la Afilisti.
“Ndidzakuwononga
ndipo palibe amene adzatsale.”
6 Dziko la mʼmbali mwa nyanja, kumene kumakhala Akereti,
lidzakhala malo a abusa ndi la makola a nkhosa.
7 Malowa adzakhala a anthu otsala a nyumba ya Yuda;
adzapezako msipu.
Nthawi ya madzulo adzagona
mʼnyumba za Asikeloni.
Yehova Mulungu wawo adzawasamalira;
adzabwezeretsa mtendere wawo.
Za Mowabu ndi Amoni
8 “Ndamva kunyoza kwa Mowabu
ndi chipongwe cha Amoni,
amene ananyoza anthu anga
ndi kuopseza kuti alanda dziko lawo.
9 Choncho, pali Ine Wamoyo,”
akutero Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli,
“Ndithu, Mowabu adzasanduka ngati Sodomu,
Amoni adzasanduka ngati Gomora;
malo a zomeramera ndi maenje a mchere,
dziko la bwinja mpaka muyaya.
Anthu anga otsala adzawafunkha;
opulumuka a mtundu wanga adzalandira dziko lawo.”
10 Ichi ndi chimene adzalandire chifukwa cha kunyada kwawo,
chifukwa chonyoza ndi kuchitira chipongwe anthu a Yehova Wamphamvuzonse.
11 Yehova adzawachititsa mantha kwambiri
pamene adzawononga milungu yonse ya mʼdzikomo.
Ndipo mitundu ya anthu pa dziko lonse idzamulambira,
uliwonse ku dziko la kwawo.
Za Kusi
12 “Inunso anthu a ku Kusi,
mudzaphedwa ndi lupanga.”
Za Asiriya
13 Yehova adzatambasulira dzanja lake kumpoto
ndi kuwononga Asiriya,
kusiya Ninive atawonongekeratu
ndi owuma ngati chipululu.
14 Nkhosa ndi ngʼombe zidzagona pansi kumeneko,
pamodzi ndi nyama zakuthengo za mtundu uliwonse.
Akadzidzi a mʼchipululu ndi akanungu
adzakhala pa nsanamira zake.
Kulira kwawo kudzamveka mʼmazenera,
mʼmakomo mwawo mudzakhala zinyalala zokhazokha,
nsanamira za mkungudza zidzakhala poonekera.
15 Umenewu ndiye mzinda wosasamala
umene kale unali wotetezedwa.
Unkanena kuti mu mtima mwake,
“Ine ndine, ndipo palibenso wina wondiposa.”
Taonani lero wasanduka bwinja,
kokhala nyama zakutchire!
Onse owudutsa akuwunyoza
ndi kupukusa mitu yawo.
Zephaniah 2
King James Version
2 Gather yourselves together, yea, gather together, O nation not desired;
2 Before the decree bring forth, before the day pass as the chaff, before the fierce anger of the Lord come upon you, before the day of the Lord's anger come upon you.
3 Seek ye the Lord, all ye meek of the earth, which have wrought his judgment; seek righteousness, seek meekness: it may be ye shall be hid in the day of the Lord's anger.
4 For Gaza shall be forsaken, and Ashkelon a desolation: they shall drive out Ashdod at the noon day, and Ekron shall be rooted up.
5 Woe unto the inhabitants of the sea coast, the nation of the Cherethites! the word of the Lord is against you; O Canaan, the land of the Philistines, I will even destroy thee, that there shall be no inhabitant.
6 And the sea coast shall be dwellings and cottages for shepherds, and folds for flocks.
7 And the coast shall be for the remnant of the house of Judah; they shall feed thereupon: in the houses of Ashkelon shall they lie down in the evening: for the Lord their God shall visit them, and turn away their captivity.
8 I have heard the reproach of Moab, and the revilings of the children of Ammon, whereby they have reproached my people, and magnified themselves against their border.
9 Therefore as I live, saith the Lord of hosts, the God of Israel, Surely Moab shall be as Sodom, and the children of Ammon as Gomorrah, even the breeding of nettles, and saltpits, and a perpetual desolation: the residue of my people shall spoil them, and the remnant of my people shall possess them.
10 This shall they have for their pride, because they have reproached and magnified themselves against the people of the Lord of hosts.
11 The Lord will be terrible unto them: for he will famish all the gods of the earth; and men shall worship him, every one from his place, even all the isles of the heathen.
12 Ye Ethiopians also, ye shall be slain by my sword.
13 And he will stretch out his hand against the north, and destroy Assyria; and will make Nineveh a desolation, and dry like a wilderness.
14 And flocks shall lie down in the midst of her, all the beasts of the nations: both the cormorant and the bittern shall lodge in the upper lintels of it; their voice shall sing in the windows; desolation shall be in the thresholds; for he shall uncover the cedar work.
15 This is the rejoicing city that dwelt carelessly, that said in her heart, I am, and there is none beside me: how is she become a desolation, a place for beasts to lie down in! every one that passeth by her shall hiss, and wag his hand.
Zephaniah 2
English Standard Version
Judgment on Judah's Enemies
2 Gather together, yes, gather,
O (A)shameless nation,
2 (B)before the decree takes effect[a]
—before the day passes away (C)like chaff—
(D)before there comes upon you
the burning anger of the Lord,
before there comes upon you
the day of the anger of the Lord.
3 (E)Seek the Lord, (F)all you humble of the land,
who do his just commands;[b]
(G)seek righteousness; seek humility;
(H)perhaps (I)you may be hidden
on the day of the anger of the Lord.
4 (J)For Gaza shall be deserted,
and Ashkelon shall become a desolation;
Ashdod's people shall be driven out at noon,
and Ekron shall be uprooted.
5 Woe to (K)you inhabitants of the seacoast,
you nation of (L)the Cherethites!
(M)The word of the Lord is against you,
(N)O Canaan, land of the Philistines;
and I will destroy you (O)until no inhabitant is left.
6 (P)And you, O seacoast, (Q)shall be pastures,
with meadows[c] for shepherds
and folds for flocks.
7 (R)The seacoast shall become the possession
of (S)the remnant of the house of Judah,
(T)on which they shall graze,
and in the houses of Ashkelon
they shall lie down at evening.
For the Lord their God (U)will be mindful of them
and (V)restore their fortunes.
8 “I have heard (W)the taunts of Moab
and (X)the revilings of the Ammonites,
how they have taunted my people
and made boasts (Y)against their territory.
9 Therefore, (Z)as I live,” declares the Lord of hosts,
the God of Israel,
“Moab shall become (AA)like Sodom,
and the Ammonites (AB)like Gomorrah,
a land possessed by nettles and salt pits,
and a waste forever.
The remnant of my people shall plunder them,
and the survivors of my nation shall possess them.”
10 This shall be their lot in return (AC)for their pride,
because they taunted and boasted
against the people of the Lord of hosts.
11 The Lord will be awesome against them;
(AD)for he will famish all the gods of the earth,
and (AE)to him shall bow down,
each in its place,
all (AF)the lands of the nations.
12 (AG)You also, O Cushites,
shall be slain by my sword.
13 And he will stretch out his hand against the north
(AH)and destroy Assyria,
and he (AI)will make Nineveh a desolation,
a dry waste like the desert.
14 (AJ)Herds shall lie down in her midst,
all kinds of beasts;[d]
(AK)even the owl and the hedgehog[e]
shall lodge in her capitals;
a voice shall hoot in the window;
devastation will be on the threshold;
for (AL)her cedar work will be laid bare.
15 This is the exultant city
(AM)that lived securely,
that said in her heart,
“I am, and there is no one else.”
What a desolation she has become,
(AN)a lair for wild beasts!
(AO)Everyone who passes by her
hisses and (AP)shakes his fist.
Footnotes
- Zephaniah 2:2 Hebrew gives birth
- Zephaniah 2:3 Or who carry out his judgment
- Zephaniah 2:6 Or caves
- Zephaniah 2:14 Hebrew beasts of every nation
- Zephaniah 2:14 The identity of the animals rendered owl and hedgehog is uncertain
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
The ESV® Bible (The Holy Bible, English Standard Version®), © 2001 by Crossway, a publishing ministry of Good News Publishers. ESV Text Edition: 2025.
