Yobu 3:21-23
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
21 kwa iwo amene amalakalaka imfa imene sibwera,
amene amayifunafuna imfayo kupambana chuma chobisika,
22 amene amakondwa ndi kusangalala
akamalowa mʼmanda?
23 Chifuwa chiyani moyo umaperekedwa kwa munthu
amene njira yake yabisika,
amene Mulungu wamuzinga ponseponse?
Job 3:21-23
New International Version
Job 3:21-23
King James Version
21 Which long for death, but it cometh not; and dig for it more than for hid treasures;
22 Which rejoice exceedingly, and are glad, when they can find the grave?
23 Why is light given to a man whose way is hid, and whom God hath hedged in?
Read full chapterThe Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.